1Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi
2Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti,
3Mulungu wathu ali kumwamba;
4Koma mafano awo ndi siliva ndi golide,
5Pakamwa ali napo koma sayankhula,
6makutu ali nawo koma samva,
7manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu;
8Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo,
9Inu Aisraeli, dalirani Yehova;
10Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova;
11Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova;
12Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa:
13adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova;
14Yehova akuwonjezereni madalitso;
15Mudalitsidwe ndi Yehova,
16Kumwamba ndi kwa Yehova,
17Si anthu akufa amene amatamanda Yehova,
18ndi ife amene timatamanda Yehova,