We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 115

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 114 Masalimo Masalimo 116 →

1Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi

2Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti,

3Mulungu wathu ali kumwamba;

4Koma mafano awo ndi siliva ndi golide,

5Pakamwa ali napo koma sayankhula,

6makutu ali nawo koma samva,

7manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu;

8Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo,

9Inu Aisraeli, dalirani Yehova;

10Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova;

11Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova;

12Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa:

13adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova;

14Yehova akuwonjezereni madalitso;

15Mudalitsidwe ndi Yehova,

16Kumwamba ndi kwa Yehova,

17Si anthu akufa amene amatamanda Yehova,

18ndi ife amene timatamanda Yehova,

← Masalimo 114 Masalimo Masalimo 116 →