1Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga;
2Pakuti ananditchera khutu,
3Zingwe za imfa zinandizinga,
4Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova:
5Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama
6Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima;
7Pumula iwe moyo wanga,
8Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa,
9kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova
10Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati,
11Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati,
12Ndingamubwezere chiyani Yehova,
13Ndidzakweza chikho cha chipulumutso
14Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova
15Imfa ya anthu oyera mtima
16Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu:
17Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu
18Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova
19mʼmabwalo a nyumba ya Yehova,