We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 116

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 115 Masalimo Masalimo 117 →

1Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga;

2Pakuti ananditchera khutu,

3Zingwe za imfa zinandizinga,

4Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova:

5Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama

6Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima;

7Pumula iwe moyo wanga,

8Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa,

9kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova

10Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati,

11Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati,

12Ndingamubwezere chiyani Yehova,

13Ndidzakweza chikho cha chipulumutso

14Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova

15Imfa ya anthu oyera mtima

16Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu:

17Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu

18Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova

19mʼmabwalo a nyumba ya Yehova,

← Masalimo 115 Masalimo Masalimo 117 →