1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,
2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,
3Nyanja inaona ndi kuthawa,
4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,
5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?
6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,
7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,
8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,