We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 113

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 112 Masalimo Masalimo 114 →

1Tamandani Yehova.

2Yehova atamandidwe,

3Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake,

4Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse,

5Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu,

6amene amawerama pansi kuyangʼana

7Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi

8amawakhazika pamodzi ndi mafumu,

9Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake

← Masalimo 112 Masalimo Masalimo 114 →