1Tamandani Yehova.
2Yehova atamandidwe,
3Kuyambira ku matulukiro a dzuwa mpaka ku malowero ake,
4Yehova wakwezeka pa anthu a mitundu yonse,
5Ndani wofanana ndi Yehova Mulungu wathu,
6amene amawerama pansi kuyangʼana
7Iye amakweza munthu wosauka kuchoka pa fumbi
8amawakhazika pamodzi ndi mafumu,
9Amakhazikitsa mayi wosabereka mʼnyumba yake