We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 112

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 111 Masalimo Masalimo 113 →

1Tamandani Yehova.

2Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;

3Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,

4Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;

5Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,

6Ndithu sadzagwedezeka;

7Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;

8Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;

9Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,

10Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;

← Masalimo 111 Masalimo Masalimo 113 →