We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 111

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 110 Masalimo Masalimo 112 →

1Tamandani Yehova.

2Ntchito za Yehova nʼzazikulu;

3Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,

4Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;

5Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;

6Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,

7Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;

8Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,

9Iyeyo amawombola anthu ake;

10Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;

← Masalimo 110 Masalimo Masalimo 112 →