1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,
2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;
3Ankhondo ako adzakhala odzipereka
4Yehova walumbira
5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;
6Adzaweruza anthu a mitundu ina,
7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;