1Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu;
2Dzukani, zeze ndi pangwe!
3Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;
4Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba;
5Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,
6Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja
7Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:
8Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;
9Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo
10Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa?
11Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana
12Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani,
13Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano,