We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 108

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 107 Masalimo Masalimo 109 →

1Mtima wanga ndi wokhazikika, Inu Mulungu;

2Dzukani, zeze ndi pangwe!

3Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina;

4Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba;

5Kwezekani Inu Mulungu, kuposa mayiko akumwamba,

6Tipulumutseni ndi kutithandiza ndi dzanja lanu lamanja

7Mulungu wayankhula kuchokera ku malo ake opatulika:

8Giliyadi ndi wanga, Manase ndi wanganso;

9Mowabu ndi mbale yanga yosambiramo

10Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa?

11Kodi sindinu Mulungu, Inu amene mwatikana

12Tithandizeni ife kulimbana ndi mdani,

13Chifukwa cha Mulungu wathu, ife tidzapeza chipambano,

← Masalimo 107 Masalimo Masalimo 109 →