We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 107

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 106 Masalimo Masalimo 108 →

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino;

2Owomboledwa a Yehova anene zimenezi

3iwo amene anawasonkhanitsa kuchokera ku mayiko,

4Ena anayendayenda mʼchipululu mopanda kanthu,

5Iwo anamva njala ndi ludzu,

6Pamenepo analirira Yehova mʼmavuto awo

7Iye anawatsogolera mʼnjira yowongoka

8Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

9pakuti Iye wapha ludzu la munthu womva ludzu

10Ena anakhala mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu,

11pakuti iwowo anawukira mawu a Mulungu

12Kotero Iye anawapereka kuti agwire ntchito yakalavulagaga;

13Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

14Yehova anawatulutsa mu mdima ndi mʼchisoni chachikulu

15Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

16pakuti Iye amathyola zipata zamkuwa

17Ena anakhala zitsiru chifukwa cha njira zawo zowukira,

18Iwo ananyansidwa ndi chakudya chilichonse

19Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

20Iye anatumiza mawu ake ndi kuwachiritsa;

21Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

22Apereke nsembe yachiyamiko

23Ena anayenda pa nyanja mʼsitima zapamadzi;

24Anaona ntchito za Yehova,

25Pakuti Iye anayankhula ndi kuwutsa mphepo yamkuntho

26Sitima za pamadzizo zinatukulidwa mmwamba ndi kutsikira pansi pakuya;

27Anachita chizungulire ndi kudzandira ngati anthu oledzera;

28Pamenepo analirira Yehova mʼmasautso awo

29Yehova analetsa namondwe,

30Anali osangalala pamene kunakhala bata,

31Ayamike Yehova chifukwa cha chikondi chake chosatha

32Akuze Iye mu msonkhano wa anthu

33Iye anasandutsa mitsinje kukhala chipululu,

34ndiponso nthaka yachonde kukhala nthaka yamchere,

35Anasandutsa chipululu kukhala mayiwe a madzi

36kumeneko Iye anabweretsa anthu anjala kuti azikhalako,

37Anafesa mbewu mʼminda ndi kudzala mipesa

38Yehova anawadalitsa, ndipo chiwerengero chawo chinachuluka kwambiri,

39Kenaka chiwerengero chawo chinachepa ndipo iwo anatsitsidwa

40Iye amene amakhuthulira mʼnyozo pa olemekezeka

41Koma Iyeyo anakweza anthu osowa kuchoka ku masautso awo

42Anthu olungama mtima amaona ndi kusangalala,

43Aliyense wanzeru asamalitse zinthu zimenezi

← Masalimo 106 Masalimo Masalimo 108 →