1Tamandani Yehova.
2Ndani angathe kufotokoza za ntchito zamphamvu za Yehova
3Odala ndi amene amasunga chilungamo,
4Mundikumbukire Yehova, pamene mukuonetsa kukoma mtima kwanu kwa anthu anu,
5kuti ndidzasangalale ndi chuma cha anthu anu osankhika,
6Ife tachimwa monga momwe anachitira makolo athu;
7Pamene makolo athu anali mu Igupto,
8Komabe Iye anawapulumutsa chifukwa cha dzina lake,
9Anadzudzula Nyanja Yofiira, ndipo inawuma;
10Anawapulumutsa mʼdzanja la amaliwongo;
11Madzi anamiza adani awo,
12Kenaka iwo anakhulupirira malonjezo ake
13Koma posachedwa anayiwala zimene Iye anachita,
14Mʼchipululu, anadzipereka ku zilakolako zawo;
15Choncho Iye anawapatsa chimene anapempha,
16Mʼmisasa, anachitira nsanje Mose ndi Aaroni,
17Nthaka inatsekuka ndipo inameza Datani;
18Moto unayaka pakati pa otsatira awo;
19Iwo anapanga mwana wangʼombe pa Horebu
20Anasinthanitsa ulemerero wawo
21Anayiwala Mulungu amene anawapulumutsa,
22zozizwitsa mʼdziko la Hamu
23Choncho Iye anawawuza kuti adzawawononga,
24Motero iwo ananyoza dziko lokoma;
25Anangʼungʼudza mʼmatenti mwawo
26Kotero Iye analumbira atakweza dzanja lake,
27kuchititsa kuti zidzukulu zawo zifere pakati pa anthu a mitundu ina
28Iwo anayamba kupembedza Baala-Peori
29anaputa mkwiyo wa Yehova pa machitidwe awo oyipa,
30Koma Finehasi anayimirira ndi kulowererapo,
31Chimenechi ndicho chinayesedwa chilungamo chake,
32Pa madzi a ku Meriba iwo anakwiyitsa Yehova
33pakuti iwowo anawukira mzimu wa Mulungu,
34Aisraeliwo sanawononge mitundu ya anthu
35Koma anasakanizana ndi anthu a mitundu inayo
36Ndipo anapembedza mafano awo,
37Anapereka nsembe ana awo aamuna
38Anakhetsa magazi a anthu osalakwa,
39Iwo anadzidetsa okha ndi zimene anachita;
40Tsono Yehova anakwiya ndi anthu ake
41Iye anawapereka kwa anthu a mitundu ina,
42Adani awo anawazunza
43Iye ankawapulumutsa nthawi zambiri,
44Koma Iye anaona kuzunzika kwawo
45Chifukwa cha iwo Iye anakumbukira pangano lake
46Iye anachititsa kuti amene anawagwira iwo ukapolo
47Tipulumutseni Inu Yehova Mulungu wathu,
48Atamandike Yehova, Mulungu wa Israeli,