1Sonkhanani pamodzi, sonkhanani pamodzi,
2isanafike nthawi yachiweruzo,
3Funafunani Yehova, inu nonse odzichepetsa a mʼdziko,
4Gaza adzasiyidwa
5Tsoka inu okhala mʼmbali mwa nyanja,
6Dziko la mʼmbali mwa nyanja, kumene kumakhala Akereti,
7Malowa adzakhala a anthu otsala a nyumba ya Yuda;
8“Ndamva kunyoza kwa Mowabu
9Choncho, pali Ine Wamoyo,”
10Ichi ndi chimene adzalandire chifukwa cha kunyada kwawo,
11Yehova adzawachititsa mantha kwambiri
12“Inunso anthu a ku Kusi,
13Yehova adzatambasulira dzanja lake kumpoto
14Nkhosa ndi ngʼombe zidzagona pansi kumeneko,
15Umenewu ndiye mzinda wosasamala