1Tsoka kwa mzinda wa anthu opondereza,
2Sumvera aliyense,
3Akuluakulu ake ali ngati mikango yobuma,
4Aneneri ake ndi odzikuza;
5Yehova amene ali pakati pawo ndi wolungama;
6“Ndachotseratu mitundu ya anthu;
7Ndinati,
8Choncho mundidikire,” akutero Yehova,
9“Pamenepo ndidzayeretsa milomo ya anthu a mitundu yonse
10Kuchokera kutsidya kwa mitsinje ya ku Kusi
11Tsiku limenelo simudzachita manyazi
12Koma ndidzasiya pakati panu
13Aisraeli otsala sadzachitanso zolakwika;
14Imba, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni;
15Yehova wachotsa chilango chako,
16Pa tsiku limenelo adzanena kwa Yerusalemu kuti,
17Yehova Mulungu wako ali pakati pako,
18“Ndidzakuchotserani zowawa
19Taonani, nthawi imeneyo ndidzathana ndi
20Pa nthawi imeneyo ndidzakusonkhanitsani;