We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Zefaniya 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Zefaniya Zefaniya 2 →

1Yehova anayankhula ndi Zefaniya mwana wa Kusi, mwana wa Gedaliya, mwana wa Amariya, mwana wa Hezekiya pa nthawi ya Yosiya, mwana wa Amoni, mfumu ya Yuda.

2“Ndidzawononga kotheratu zinthu zonse

3“Ndidzawononga anthu pamodzi ndi nyama zomwe;

4Ndidzatambasula dzanja langa pa Yuda

5amene amagwada pa madenga a nyumba zawo

6amene abwerera mʼmbuyo osatsata Yehova,

7Khalani chete pamaso pa Ambuye Yehova,

8Pa tsiku la nsembe ya Yehova

9Pa tsiku limenelo ndidzalanga

10“Pa tsiku limenelo,” akutero Yehova,

11Lirani mwachisoni, inu amene mumakhala kumene kuli msika;

12Pa nthawi imeneyo ndidzafufuzafufuza mu Yerusalemu ndi nyale

13Chuma chawo chidzafunkhidwa,

14Tsiku lalikulu la Yehova layandikira,

15Tsiku limenelo lidzakhala la ukali,

16Tsiku loliza lipenga ndi la mfuwu wankhondo,

17Ndidzabweretsa msautso pa anthu

18Ngakhale siliva wawo kapena golide wawo

Zefaniya Zefaniya 2 →