1Yehova anayankhula ndi Zefaniya mwana wa Kusi, mwana wa Gedaliya, mwana wa Amariya, mwana wa Hezekiya pa nthawi ya Yosiya, mwana wa Amoni, mfumu ya Yuda.
2“Ndidzawononga kotheratu zinthu zonse
3“Ndidzawononga anthu pamodzi ndi nyama zomwe;
4Ndidzatambasula dzanja langa pa Yuda
5amene amagwada pa madenga a nyumba zawo
6amene abwerera mʼmbuyo osatsata Yehova,
7Khalani chete pamaso pa Ambuye Yehova,
8Pa tsiku la nsembe ya Yehova
9Pa tsiku limenelo ndidzalanga
10“Pa tsiku limenelo,” akutero Yehova,
11Lirani mwachisoni, inu amene mumakhala kumene kuli msika;
12Pa nthawi imeneyo ndidzafufuzafufuza mu Yerusalemu ndi nyale
13Chuma chawo chidzafunkhidwa,
14Tsiku lalikulu la Yehova layandikira,
15Tsiku limenelo lidzakhala la ukali,
16Tsiku loliza lipenga ndi la mfuwu wankhondo,
17Ndidzabweretsa msautso pa anthu
18Ngakhale siliva wawo kapena golide wawo