1Nzeru inamanga nyumba yake;
2Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake;
3Nzeruyo inatuma adzakazi ake,
4“Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!”
5“Bwerani, dzadyeni chakudya changa
6Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo;
7Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo;
8Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe;
9Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru;
10Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru;
11Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka,
12Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa;
13Uchitsiru ndi mkazi waphokoso,
14Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake,
15kuti aziyitana anthu ongodutsa,
16Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,”
17“Madzi akuba ndiye amatsekemera;
18Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko,