We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 9

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 8 Miyambo Miyambo 10 →

1Nzeru inamanga nyumba yake;

2Inapha ziweto zake ndipo yasakaniza vinyo wake;

3Nzeruyo inatuma adzakazi ake,

4“Aliyense amene ali munthu wamba, abwere kuno!”

5“Bwerani, dzadyeni chakudya changa

6Lekani zopusa zanu kuti mukhale ndi moyo;

7Aliyense amene amayesa kukonza munthu wonyoza amadziputira minyozo;

8Usadzudzule munthu wonyoza kuti angadzadane nawe;

9Ukalangiza munthu wanzeru ndiye adzapitirira kukhala wanzeru;

10Kuopa Yehova ndiye chiyambi cha nzeru;

11Chifukwa cha ine nzeru, masiku ako adzachuluka,

12Ngati ndiwe wanzeru, nzeru yakoyo idzakupindulitsa;

13Uchitsiru ndi mkazi waphokoso,

14Iye amakhala pa mpando, pa khomo la nyumba yake,

15kuti aziyitana anthu ongodutsa,

16Amati, “Onse amene ndi anthu wamba abwere kuno,”

17“Madzi akuba ndiye amatsekemera;

18Koma amunawo sadziwa kuti akufa ali kale komweko,

← Miyambo 8 Miyambo Miyambo 10 →