1Miyambo ya Solomoni:
2Chuma chochipeza mwachinyengo sichipindulitsa,
3Yehova salola kuti munthu wolungama azikhala ndi njala;
4Wochita zinthu mwaulesi amasauka,
5Amene amakolola nthawi yachilimwe ndi mwana wanzeru,
6Madalitso amakhala pa mutu wa munthu wolungama,
7Munthu wolungama anzake adzamukumbukira ngati mdalitso,
8Munthu wa mtima wanzeru amasamala malamulo,
9Munthu woyenda mwangwiro amayenda mosatekeseka;
10Aliyense wotsinzinira maso mwachinyengo amabweretsa mavuto,
11Pakamwa pa munthu wolungama ndi kasupe wamoyo,
12Udani umawutsa mikangano,
13Nzeru imapezeka pa milomo ya munthu wozindikira zinthu,
14Anzeru amasunga chidziwitso
15Chuma cha munthu wolemera
16Moyo ndiye malipiro a munthu wolungama,
17Wosamalira malangizo amayenda mʼnjira ya moyo,
18Amene amabisa chidani chake ndi munthu wonama,
19Mawu akachuluka zolakwa sizisowa,
20Mawu a munthu wolungama ali ngati siliva wabwino kwambiri,
21Milomo ya anthu olungama imalimbikitsa ambiri;
22Mdalitso wa Yehova ndiwo umabweretsa chuma,
23Kwa chitsiru kuchita zinthu zoyipa ndiye chinthu chomusangalatsa,
24Chimene munthu woyipa amachiopa chidzamuchitikira;
25Pamene namondwe wawomba, anthu oyipa amachotsedwa,
26Momwe amakhalira vinyo wosasa mʼkamwa ndi momwe umakhalira utsi mʼmaso,
27Kuopa Yehova kumatalikitsa moyo;
28Chiyembekezo cha olungama chimapatsa chimwemwe,
29Njira za Yehova ndi linga loteteza anthu ochita zabwino,
30Munthu wolungama sadzachotsedwa, pamalo pake
31Pakamwa pa munthu wolungama pamatulutsa za nzeru,
32Milomo ya anthu olungama imadziwa zoyenera kuyankhula,