We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 11

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 10 Miyambo Miyambo 12 →

1Muyeso wachinyengo Yehova umamunyansa,

2Kunyada kukalowa, pamafikanso manyazi,

3Ungwiro wa anthu olungama umawatsogolera,

4Chuma sichithandiza pa tsiku lawukali wa Mulungu,

5Chilungamo cha anthu angwiro chimawongolera moyo wawo,

6Chilungamo cha anthu oyera mtima chimawapulumutsa,

7Pamene munthu woyipa wafa, chiyembekezo chake chimathanso.

8Munthu wolungama amapulumutsidwa ku mavuto,

9Munthu wosapembedza amawononga mnansi wake ndi pakamwa pake,

10Anthu olungama zinthu zikamawayendera bwino, mzinda wonse umakondwera,

11Mzinda umakwezeka chifukwa cha madalitso a anthu oyera mtima,

12Munthu wonyoza mnzake ndi wopanda nzeru,

13Amene amanka nachita ukazitape amawulula zinsinsi;

14Pakasoweka uphungu mtundu wa anthu umagwa;

15Woperekera mlendo chikole adzapeza mavuto,

16Mkazi wodekha amalandira ulemu,

17Munthu wachifundo amadzipindulira zabwino

18Munthu woyipa amalandira malipiro wopanda phindu,

19Munthu wochita za chilungamo amapeza moyo,

20Yehova amanyansidwa ndi anthu a mtima wokhotakhota

21Zoonadi, anthu oyipa adzalangidwa,

22Monga imaonekera mphete yagolide ikakhala pa mphuno ya nkhumba,

23Zokhumba za anthu olungama zimathera pa zabwino zokhazokha,

24Munthu wina amapatsako anzake zinthu mwaufulu nʼkumangolemererabe;

25Munthu wopereka mowolowamanja adzalemera;

26Anthu amatemberera womana anzake chakudya,

27Iye amene amafunafuna zabwino mwakhama amapeza zabwinozo,

28Aliyense amene amadalira chuma chake adzafota,

29Wovutitsa a mʼnyumba mwake adzalowa mʼmavuto,

30Chipatso cha ntchito zabwino ndi moyo,

31Ngati anthu olungama amalandira mphotho zawo pa dziko lapansi,

← Miyambo 10 Miyambo Miyambo 12 →