We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 12

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 11 Miyambo Miyambo 13 →

1Munthu amene amakonda mwambo amakonda kudziwa zinthu,

2Munthu wabwino amapeza kuyanja pamaso pa Yehova,

3Munthu sangakhazikike bwino pochita zoyipa,

4Mkazi wakhalidwe labwino ali ngati chipewa chaufumu kwa mwamuna wake,

5Maganizo a anthu olungama ndi owongoka,

6Mawu a anthu oyipa ndi ophetsa,

7Anthu oyipa amagonjetsedwa ndipo amayiwalika,

8Munthu amatamandidwa malinga ndi nzeru zake,

9Nʼkwabwino kukhala munthu wonyozeka koma wodzigwirira ntchito nʼkukhala ndi zonse zofunika,

10Munthu wolungama amasamalira moyo wa ziweto zake,

11Wolima mʼmunda mwake mwakhama adzakhala ndi chakudya chochuluka,

12Munthu woyipa amalakalaka zofunkha za anthu oyipa,

13Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa;

14Munthu amakhala ndi zabwino zambiri chifukwa cha mawu ake

15Zochita za chitsiru mwini wakeyo amaziona ngati zabwino,

16Mkwiyo wa chitsiru umadziwika nthawi yomweyo,

17Woyankhula zoona amapereka umboni woona,

18Munthu woyankhula mosasamala mawu ake amalasa ngati lupanga,

19Mawu woona amakhala mpaka muyaya

20Mʼmitima ya anthu amene amakonza zoyipa muli chinyengo;

21Palibe choyipa chimene chimagwera munthu wolungama,

22Pakamwa pa bodza pamamunyansa Yehova,

23Munthu wochenjera amabisa nzeru zake,

24Ogwira ntchito mwakhama adzalamulira,

25Nkhawa imakhala ngati katundu wolemera mu mtima mwa munthu,

26Munthu wolungama amatsogolera mnansi wake,

27Munthu waulesi sapeza chimene akufuna,

28Mʼnjira yachilungamo muli moyo;

← Miyambo 11 Miyambo Miyambo 13 →