We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 8

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 7 Miyambo Miyambo 9 →

1Kodi nzeru sikuyitana?

2Nzeru imayima pa zitunda mʼmbali mwa njira,

3Imafuwula pafupi ndi zipata zolowera mu mzinda,

4Inu anthu, ndikuyitana inu;

5Inu amene simudziwa kanthunu khalani ochenjera;

6Mverani, pakuti ndikukuwuzani zinthu zofunika kwambiri;

7Pakamwa panga pamayankhula zoona

8Mawu onse a pakamwa panga ndi olungama;

9Kwa anthu ozindikira, mawu anga onse ndi woona;

10Landirani malangizo anga mʼmalo mwa siliva,

11Paja nzeru ndi yabwino kwambiri kuposa miyala yamtengowapatali,

12Ine nzeru, ndimakhala pamodzi ndi kuchenjera.

13Kuopa Yehova ndiko kudana ndi zoyipa.

14Ndine mwini uphungu ndi maganizo abwino;

15Ndine amene ndimathandiza mafumu kulamulira.

16Ndine amene ndimathandiza akalonga polamula.

17Ndimakonda amene amandikonda,

18Ine ndili ndi chuma ndi ulemu,

19Chipatso changa ndi chabwino kuposa golide, ngakhale golide wosalala;

20Ndimachita zinthu zolungama.

21Ndimapereka chuma kwa amene amandikonda

22“Yehova anandilenga ine nzeru monga ntchito yake yoyamba.

23Ndinapangidwa kalekalelo,

24Nyanja, akasupe odzaza ndi madzi,

25Mapiri asanakhazikitsidwe pa malo awo,

26lisanalengedwe dziko lapansi ndi minda yake;

27Ine ndinalipo pamene Yehova ankakhazikitsa mlengalenga,

28pamene anakhazikitsa mitambo ya mlengalenga

29pamene anayikira nyanja malire

30Tsono ine ndinali pambali pake ngati mmisiri;

31Ndinkasangalala ndi dziko lake lonse

32“Ndiye tsono ana inu, ndimvereni;

33Mverani malangizo anga kuti mukhale ndi nzeru;

34Wodala munthu amene amandimvera,

35Paja aliyense amene apeza ine wapeza moyo

36Koma amene alephera kundipeza, amadzipweteka yekha;

← Miyambo 7 Miyambo Miyambo 9 →