1Mwana wanga, mvera mawu anga;
2Utsate malamulo anga ndipo udzakhala ndi moyo;
3Uchite ngati wawamangirira pa zala zako,
4Nzeru uyiwuze kuti, “Iwe ndiwe mlongo wanga,”
5Zidzakuteteza kwa mkazi wachigololo
6Tsiku lina pa zenera la nyumba yanga
7Ndinaona pakati pa anthu opusa,
8Iye ankayenda njira yodutsa pafupi ndi nyumba ya mkaziyo,
9Inali nthawi yachisisira madzulo,
10Ndipo mkaziyo anadzakumana naye,
11(Mkaziyo ndi wolongolola ndiponso nkhutukumve,
12Mwina umupeza pa msewu, mwina umupeza pa msika,
13Tsono amagwira mnyamatayo ndi kupsompsona
14“Ndinayenera kupereka nsembe zachiyanjano.
15Choncho ndinabwera kudzakumana nawe;
16Pa bedi panga ndayalapo
17Pa bedi panga ndawazapo zonunkhira
18Bwera, tiye tikhale malo amodzi kukondwerera chikondi mpaka mmawa;
19Mwamuna wanga kulibe ku nyumbako;
20Anatenga thumba la ndalama
21Ndi mawu ake onyengerera amamukakamiza mnyamatayo;
22Nthawi yomweyo chitsiru chimamutsatira mkaziyo
23mpaka muvi utalasa chiwindi chake,
24Tsono ana inu, ndimvereni;
25Musatengeke mtima ndi njira za mkazi ameneyu;
26Paja iye anagwetsa anthu ambiri;
27Nyumba yake ndi njira yopita ku manda,