We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 2 Miyambo Miyambo 4 →

1Mwana wanga, usayiwale malangizo anga,

2Ukatero zaka za moyo wako zidzachuluka

3Makhalidwe ochitira ena chifundo ndi owonetsa kukhulupirika asakuchokere.

4Ukatero udzapeza kuyanja ndi mbiri yabwino

5Uzikhulupirira Yehova ndi mtima wako wonse

6Pa zochita zako zonse uvomereze kuti Mulungu alipo,

7Usamadzione ngati wa nzeru.

8Ukatero thupi lako lidzakhala la moyo wabwino

9Uzilemekeza Yehova ndi chuma chako chonse;

10Ukatero nkhokwe zako zidzadzaza ndi zinthu zambiri,

11Mwana wanga usanyoze malangizo a Yehova,

12Paja Yehova amadzudzula amene amamukonda,

13Wodala munthu amene wapeza nzeru,

14pakuti phindu la nzeru ndi labwino kuposa la siliva,

15Nzeru ndi yoposa miyala yamtengowapatali;

16Mʼdzanja lake lamanja muli moyo wautali;

17Njira zake ndi njira zosangalatsa,

18Nzeru ili ngati mtengo wopatsa moyo kwa oyigwiritsitsa;

19Yehova anakhazikitsa dziko lapansi pogwiritsa ntchito nzeru.

20Mwa nzeru zake Yehova anatumphutsa madzi kuchokera mʼnthaka

21Mwana wanga usunge nzeru yeniyeni ndi khalidwe lomalingarira zinthu bwino.

22Zimenezi zidzakupatsa moyo,

23Choncho udzayenda pa njira yako mosaopa kanthu,

24pamene ugona pansi, sudzachita mantha;

25Usaope tsoka lobwera mwadzidzidzi

26pakuti Yehova adzakulimbitsa mtima

27Usaleke kuchitira zabwino amene ayenera kulandira zabwino,

28Usanene kwa mnansi wako kuti,

29Usamukonzere chiwembu mnansi wako,

30Usakangane ndi munthu wopanda chifukwa

31Usachite naye nsanje munthu wachiwawa

32Pakuti Yehova amanyansidwa ndi munthu woyipa

33Yehova amatemberera nyumba ya munthu woyipa,

34Anthu onyoza, Iye amawanyoza,

35Anthu anzeru adzalandira ulemu,

← Miyambo 2 Miyambo Miyambo 4 →