We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 1 Miyambo Miyambo 3 →

1Mwana wanga, ngati ulandira mawu anga

2ndiponso kutchera khutu lako ku nzeru

3ngati upempha kuti uzindikire zinthu

4ngati ufunafuna nzeruyo ngati siliva

5ndiye udzamvetsa bwino tanthauzo la kuopa Yehova;

6Pakuti Yehova ndiye amapereka nzeru,

7Anthu olungama zinthu zimawayendera bwino chifukwa Yehova amakhala nawo.

8pakuti ndiye mlonda wa njira zolungama.

9Choncho udzamvetsa tanthauzo la ungwiro, chilungamo,

10Pakuti nzeru idzalowa mu mtima mwako,

11Kuganizira bwino za mʼtsogolo kudzakusunga;

12Nzeru idzakupulumutsa ku mayendedwe oyipa,

13amene amasiya njira zolungama

14amene amakondwera pochita zoyipa

15Amenewa ndi anthu a njira zawo zokhotakhota,

16Nzeruyo idzakupulumutsanso kwa mkazi wachigololo;

17amene wasiya mwamuna wa chitsikana wake

18Pakuti nyumba yake imatsetserekera ku imfa;

19Opita kwa iye palibe ndi mmodzi yemwe amabwerera

20Choncho iwe uziyenda mʼnjira za anthu abwino,

21Pakuti anthu olungama ndiwo ati adzakhale mʼdziko

22Koma anthu oyipa adzachotsedwa mʼdzikomo,

← Miyambo 1 Miyambo Miyambo 3 →