1Munthu amene amawumitsabe khosi lake atadzudzulidwa kwambiri,
2Anthu olungama akamalamulira mʼdziko anthu amakondwa,
3Munthu amene amakonda nzeru amasangalatsa abambo ake,
4Mfumu imalimbitsa dziko poweruza mwachilungamo,
5Munthu woshashalika mnzake,
6Munthu woyipa amakodwa ndi machimo ake,
7Munthu wolungama amasamalira anthu osauka,
8Anthu onyoza atha kuwutsa ziwawa mu mzinda,
9Ngati munthu wanzeru atsutsana ndi chitsiru,
10Anthu okhetsa magazi amadana ndi munthu wangwiro
11Munthu wopusa amaonetsa mkwiyo wake,
12Ngati wolamulira amvera zabodza,
13Munthu wosauka ndi munthu wopondereza anzake amafanana pa kuti:
14Ngati mfumu iweruza osauka moyenera,
15Ndodo ndi chidzudzulo zimapatsa nzeru
16Oyipa akamalamulira zoyipa zimachuluka,
17Umulange mwana wako ndipo adzakupatsa mtendere
18Ngati uthenga wochokera kwa Yehova supezeka anthu amangochita zofuna zawo;
19Munthu wantchito sangalangizidwe ndi mawu okha basi;
20Ngakhale munthu wa uchitsiru nʼkuti ndiponi popeza chikhulupiriro chilipo
21Ngati munthu asasatitsa wantchito wake kuyambira ali mwana,
22Munthu wamkwiyo amayambitsa mikangano,
23Kunyada kwa munthu kudzamutsitsa,
24Woyenda ndi munthu wakuba ndi mdani wa moyo wake womwe;
25Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha,
26Anthu ambiri amafunitsitsa kuti wolamulira awakomere mtima,
27Anthu olungama amanyansidwa ndi anthu achinyengo;