1Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa,
2Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri,
3Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake
4Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa,
5Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama,
6Munthu wosauka wa makhalidwe abwino
7Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu,
8Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka
9Wokana kumvera malamulo
10Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa
11Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru,
12Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu;
13Wobisa machimo ake sadzaona mwayi,
14Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse,
15Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa
16Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza
17Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu
18Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa
19Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka,
20Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri,
21Kukondera si kwabwino,
22Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera
23Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake
24Amene amabera abambo ake kapena amayi ake
25Munthu wadyera amayambitsa mikangano,
26Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru,
27Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu,
28Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala,