We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 28

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 27 Miyambo Miyambo 29 →

1Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa,

2Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri,

3Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzake

4Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa,

5Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama,

6Munthu wosauka wa makhalidwe abwino

7Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu,

8Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochuluka

9Wokana kumvera malamulo

10Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipa

11Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru,

12Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu;

13Wobisa machimo ake sadzaona mwayi,

14Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse,

15Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusa

16Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanza

17Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthu

18Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwa

19Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka,

20Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri,

21Kukondera si kwabwino,

22Munthu wowumira amafunitsitsa kulemera

23Amene amadzudzula mnzake potsiriza pake

24Amene amabera abambo ake kapena amayi ake

25Munthu wadyera amayambitsa mikangano,

26Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru,

27Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu,

28Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala,

← Miyambo 27 Miyambo Miyambo 29 →