We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 27

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 26 Miyambo Miyambo 28 →

1Usamanyadire za mawa,

2Munthu wina akutamande, koma osati wekha;

3Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri,

4Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa.

5Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino

6Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino,

7Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi,

8Munthu amene wasochera ku nyumba kwake,

9Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima,

10Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,

11Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga;

12Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,

13Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;

14Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri,

15Mkazi wolongolola ali ngati

16Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo

17Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake,

18Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake,

19Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi,

20Manda sakhuta,

21Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo,

22Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo

23Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili.

24Paja chuma sichikhala mpaka muyaya,

25Pamene udzu watha, msipu nʼkumera;

26ana ankhosa adzakupatsani chovala

27Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri

← Miyambo 26 Miyambo Miyambo 28 →