1Usamanyadire za mawa,
2Munthu wina akutamande, koma osati wekha;
3Mwala ndi wolemera ndipo mchenganso ndi wolemera kwambiri,
4Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa mtima kumachititsa zoopsa.
5Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino
6Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke zili bwino,
7Iye amene wakhuta amayipidwa ndi chisa cha uchi,
8Munthu amene wasochera ku nyumba kwake,
9Mafuta ndi zonunkhira zimasangalatsa mtima,
10Usasiye bwenzi lako ndiponso bwenzi la abambo ako,
11Mwana wanga, khala wanzeru, ndipo ukondweretse mtima wanga;
12Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,
13Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;
14Ngati munthu apatsa mnzake moni mofuwula mmamawa kwambiri,
15Mkazi wolongolola ali ngati
16Kumuletsa mkazi wotereyu zimenezi zili ngati kuletsa mphepo
17Chitsulo chimanoledwa ndi chitsulo chinzake,
18Amene amasamalira mtengo wamkuyu adzadya zipatso zake,
19Monga momwe nkhope imaonekera mʼmadzi,
20Manda sakhuta,
21Siliva amasungunulira mu uvuni ndipo golide mʼngʼanjo,
22Ngakhale utakonola chitsiru mu mtondo
23Uzidziwe bwino nkhosa zako momwe zilili.
24Paja chuma sichikhala mpaka muyaya,
25Pamene udzu watha, msipu nʼkumera;
26ana ankhosa adzakupatsani chovala
27Mudzakhala ndi mkaka wambuzi wambiri