We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 26

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 25 Miyambo Miyambo 27 →

1Ngati chisanu choti mbee nthawi yachilimwe kapena mvula nthawi yokolola,

2Ngati timba wokhalira kuwuluka kapena namzeze wokhalira kuzungulirazungulira,

3Mkwapulo ndi wokwapulira kavalo, chitsulo ndi cha mʼkamwa mwa bulu,

4Usayankhe chitsiru monga mwa uchitsiru wake,

5Koma nthawi zina umuyankhe monga mwa uchitsiru wake,

6Kutuma chitsiru kuti akapereke uthenga

7Monga miyendo ya munthu wolumala imene ilibe mphamvu

8Kupereka ulemu kwa chitsiru

9Monga umachitira mtengo waminga wobaya mʼdzanja la chidakwa

10Munthu amene amalemba ntchito chitsiru chongoyendayenda,

11Chitsiru chimene chimabwerezabwereza uchitsiru wake

12Munthu wa uchitsiru aliko bwino popeza pali chiyembekezo

13Munthu waulesi amati, “Mu msewu muli mkango,

14Monga chitseko chimapita uku ndi uku pa zolumikizira zake,

15Munthu waulesi akapisa dzanja lake mu mʼbale;

16Munthu waulesi amadziyesa yekha wanzeru

17Munthu wongolowera mikangano imene si yake

18Monga munthu wamisala amene

19ndi momwe alili munthu wonamiza mnzake,

20Pakasowa nkhuni, moto umazima;

21Monga alili makala pa moto wonyeka kapena mmene zimachitira nkhuni pa moto,

22Mawu a munthu wamiseche ali ngati chakudya chokoma;

23Monga mmene chiziro chimakutira chiwiya chadothi

24Munthu wachidani amayankhula zabwino

25Ngakhale wotereyu mawu ake ali okoma, koma usamukhulupirire,

26Ngakhale amabisa chidani mochenjera,

27Ngati munthu akumba dzenje, adzagweramo yekha;

28Munthu wonama amadana ndi amene anawapweteka,

← Miyambo 25 Miyambo Miyambo 27 →