1Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.
2Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu;
3Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi,
4Chotsa zoyipa mʼsiliva
5Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu;
6Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu,
7paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,”
8usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu
9Kamba mlandu ndi mnansi wako,
10kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi
11Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera
12Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide
13Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola
14Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka
15Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu,
16Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira,
17Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako
18Munthu wochitira mnzake umboni wonama,
19Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto,
20Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni
21Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye;
22Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake,
23Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula,
24Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga
25Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali
26Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa
27Sibwino kudya uchi wambiri,
28Munthu amene samatha kudziretsa