We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 25

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 24 Miyambo Miyambo 26 →

1Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.

2Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu;

3Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi,

4Chotsa zoyipa mʼsiliva

5Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu;

6Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu,

7paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,”

8usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu

9Kamba mlandu ndi mnansi wako,

10kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi

11Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera

12Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide

13Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola

14Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka

15Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu,

16Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira,

17Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako

18Munthu wochitira mnzake umboni wonama,

19Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto,

20Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni

21Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye;

22Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake,

23Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula,

24Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga

25Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali

26Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa

27Sibwino kudya uchi wambiri,

28Munthu amene samatha kudziretsa

← Miyambo 24 Miyambo Miyambo 26 →