We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 23

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 22 Miyambo Miyambo 24 →

1Ngati ukhala pansi kuti udye pamodzi ndi wolamulira,

2ngati ndiwe munthu wadyera

3Usasirire zakudya zake,

4Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma,

5Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo.

6Usadye chakudya cha munthu waumbombo,

7paja iye ndi munthu amene

8Udzasanza zimene wadyazo

9Usayankhule munthu wopusa akumva,

10Usasunthe mwala wa mʼmalire akalekale

11paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;

12Mtima wako uzikhala pa malangizo

13Usaleke kumulangiza mwana;

14Ukamukwapula ndi tsatsa

15Mwana wanga, ngati mtima wako ukhala wanzeru,

16Mtima wanga udzakondwera

17Mtima wako usachite nsanje ndi anthu ochimwa,

18Ndithu za mʼtsogolo zilipo

19Tamvera mwana wanga, ndipo ukhale wanzeru,

20Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera

21Paja anthu oledzera ndi adyera amadzakhala amphawi

22Mvera abambo ako amene anakubala,

23Gula choonadi ndipo usachigulitse;

24Abambo a munthu wolungama ali ndi chimwemwe chachikulu;

25Abambo ndi amayi ako asangalale;

26Mwana wanga, undikhulupirire

27Paja mkazi wachiwerewere ali ngati dzenje lozama;

28Amabisala ngati mbala yachifwamba,

29Ndani ali ndi tsoka? Ndani ali ndi chisoni?

30Ndi amene amakhalitsa pa mowa,

31Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo,

32Potsiriza pake amaluma ngati njoka,

33Maso ako adzaona zinthu zachilendo

34Udzakhala ngati munthu amene ali gone pakati pa nyanja,

35Iwe udzanena kuti, “Anandimenya, koma sindinapwetekedwe!

← Miyambo 22 Miyambo Miyambo 24 →