1Ngati ukhala pansi kuti udye pamodzi ndi wolamulira,
2ngati ndiwe munthu wadyera
3Usasirire zakudya zake,
4Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma,
5Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo.
6Usadye chakudya cha munthu waumbombo,
7paja iye ndi munthu amene
8Udzasanza zimene wadyazo
9Usayankhule munthu wopusa akumva,
10Usasunthe mwala wa mʼmalire akalekale
11paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;
12Mtima wako uzikhala pa malangizo
13Usaleke kumulangiza mwana;
14Ukamukwapula ndi tsatsa
15Mwana wanga, ngati mtima wako ukhala wanzeru,
16Mtima wanga udzakondwera
17Mtima wako usachite nsanje ndi anthu ochimwa,
18Ndithu za mʼtsogolo zilipo
19Tamvera mwana wanga, ndipo ukhale wanzeru,
20Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera
21Paja anthu oledzera ndi adyera amadzakhala amphawi
22Mvera abambo ako amene anakubala,
23Gula choonadi ndipo usachigulitse;
24Abambo a munthu wolungama ali ndi chimwemwe chachikulu;
25Abambo ndi amayi ako asangalale;
26Mwana wanga, undikhulupirire
27Paja mkazi wachiwerewere ali ngati dzenje lozama;
28Amabisala ngati mbala yachifwamba,
29Ndani ali ndi tsoka? Ndani ali ndi chisoni?
30Ndi amene amakhalitsa pa mowa,
31Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo,
32Potsiriza pake amaluma ngati njoka,
33Maso ako adzaona zinthu zachilendo
34Udzakhala ngati munthu amene ali gone pakati pa nyanja,
35Iwe udzanena kuti, “Anandimenya, koma sindinapwetekedwe!