1Mbiri yabwino ndi yofunika kuposa chuma chambiri;
2Wolemera ndi wosauka ndi ofanana;
3Munthu wochenjera akaona choopsa amabisala,
4Mphotho ya munthu wodzichepetsa
5Mʼnjira za anthu oyipa muli minga ndi misampha,
6Mwana muzimuphunzitsa njira yake,
7Wolemera amalamulira wosauka,
8Amene amafesa zoyipa amakolola mavuto,
9Amene ali ndi diso lachifundo adzadalitsika,
10Chotsani munthu wonyoza, ndipo kukangana kudzatha;
11Amene amakonda kukhala woyera mtima ndi kumayankhula mawu abwino,
12Maso a Yehova amakhala pa anthu odziwa bwino zinthu,
13Munthu waulesi amati,
14Pakamwa pa mkazi wachigololo pali ngati dzenje lozama;
15Uchitsiru umakhala mu mtima mwa mwana,
16Amene amapondereza anthu osauka kuti awonjezere chuma chake,
17Utchere khutu lako ndipo umvere mawu anzeru;
18Zidzakhala zokondweretsa ngati uzisunga mu mtima mwako
19Ndakuphunzitsa zimenezi lero
20Kodi suja ndinakulembera malangizo makumi atatu
21malangizo okudziwitsa zolungama
22Mʼmphawi usamubere chifukwa ndi osauka,
23pakuti Yehova adzawateteza pa mlandu wawo
24Usapalane naye ubwenzi munthu wosachedwa kupsa mtima
25kuopa kuti iwe ungadzaphunzire njira zake
26Usakhale munthu wopereka chikole
27ngati ulephera kupeza njira yolipirira
28Usasunthe mwala wamʼmalire akalekale
29Kodi ukumuona munthu waluso pa ntchito yake?