1Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wamadzi mʼdzanja la Yehova;
2Makhalidwe a munthu amaoneka olungama kwa mwini wakeyo,
3Za chilungamo ndi zolondola
4Maso odzikuza ndi mtima wonyada,
5Zolinga za munthu wakhama zimachulukitsa zinthu zake;
6Chuma chochipeza ndi mawu onyenga ndi chosakhalitsa
7Chiwawa cha anthu oyipa chidzawawononga,
8Njira ya munthu wolakwa ndi yokhotakhota,
9Nʼkwabwino kukhala wekha pa ngodya ya denga la nyumba,
10Munthu woyipa amalakalaka zoyipa;
11Munthu wonyoza akalangidwa, anthu opusa amapeza nzeru;
12Zolingalira za munthu woyipa nʼzosabisika pamaso pa Yehova,
13Amene atsekera mʼkhutu mwake wosauka akamalira,
14Mphatso yoperekedwa mseri imathetsa mkwiyo,
15Chilungamo chikachitika anthu olungama amasangalala,
16Munthu amene amachoka pa njira ya anthu anzeru
17Aliyense wokonda zisangalalo adzasanduka mʼmphawi,
18Anthu oyipa adzakhala chowombolera cha anthu olungama
19Nʼkwabwino kukhala mʼchipululu
20Munthu wanzeru samwaza chuma chake,
21Amene amatsata chilungamo ndi kukhulupirika,
22Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu amphamvu
23Amene amagwira pakamwa pake ndi lilime lake
24Munthu wonyada ndi wodzikuza amamutcha, “Mnyodoli,”
25Chilakolako cha munthu waulesi chidzamupha yekha
26Tsiku lonse anthu oyipa amasirira zambiri,
27Nsembe ya anthu oyipa imamunyansa Yehova,
28Mboni yonama idzawonongeka,
29Munthu woyipa amafuna kudzionetsa ngati wolimba mtima,
30Palibe nzeru, palibe kumvetsa bwino, palibenso uphungu,
31Kavalo amamukonzera tsiku la nkhondo,