We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 20

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 19 Miyambo Miyambo 21 →

1Vinyo amachititsa munthu kukhala wonyoza ndipo chakumwa choledzeretsa chimachititsa munthu kukhala wolongolola;

2Ukali wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango;

3Nʼchaulemu kwa munthu kupewa mikangano,

4Munthu waulesi satipula mʼmunda pa nthawi yoyenera;

5Zolinga za mtima wa munthu zili ngati madzi akuya,

6Anthu ambiri amayankhula za kukhulupirika kwawo,

7Munthu wolungama amakhala ndi makhalidwe abwino;

8Mfumu ikhala pa mpando wake wa chiweruzo,

9Ndani amene anganene kuti, “Ndawuyeretsa mtima wanga;

10Masikelo ndi miyeso ya zinthu imene ili yachinyengo

11Ngakhale mwana amadziwika ndi zochita zake,

12Makutu amene amamva ndi maso amene amaona,

13Usakonde tulo ungasauke;

14Munthu wogula chinthu amati, “Sichabwino, sichabwino.”

15Pali golide ndi miyala yamtengowapatali,

16Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;

17Chakudya chochipeza mwachinyengo chimukomera munthu,

18Zokonzekera zimapindula utafunsira uphungu;

19Amene amanka nanena miseche amawulula zachinsinsi.

20Ngati munthu atemberera abambo ake kapena amayi ake,

21Cholowa chochipeza mofulumira poyamba,

22Usanene kuti, “Ine ndidzabwezera choyipa chimenechi!”

23Miyeso yosintha imamunyansa Yehova;

24Mayendedwe a munthu amawalamulira ndi Yehova,

25Ndi msampha kwa munthu kuyankhula mofulumira kuti “Chinthu ichi nʼchopatulika kwa Yehova,”

26Mfumu ya nzeru imapeta kwathunthu

27Mpweya wa munthu uli ngati nyale ya Yehova;

28Kukoma mtima ndi kukhulupirika ndizo zimasunga mfumu;

29Ulemerero wa achinyamata uli mu mphamvu zawo,

30Mikwingwirima yopweteka ndiyo imachotsa zoyipa,

← Miyambo 19 Miyambo Miyambo 21 →