1Vinyo amachititsa munthu kukhala wonyoza ndipo chakumwa choledzeretsa chimachititsa munthu kukhala wolongolola;
2Ukali wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango;
3Nʼchaulemu kwa munthu kupewa mikangano,
4Munthu waulesi satipula mʼmunda pa nthawi yoyenera;
5Zolinga za mtima wa munthu zili ngati madzi akuya,
6Anthu ambiri amayankhula za kukhulupirika kwawo,
7Munthu wolungama amakhala ndi makhalidwe abwino;
8Mfumu ikhala pa mpando wake wa chiweruzo,
9Ndani amene anganene kuti, “Ndawuyeretsa mtima wanga;
10Masikelo ndi miyeso ya zinthu imene ili yachinyengo
11Ngakhale mwana amadziwika ndi zochita zake,
12Makutu amene amamva ndi maso amene amaona,
13Usakonde tulo ungasauke;
14Munthu wogula chinthu amati, “Sichabwino, sichabwino.”
15Pali golide ndi miyala yamtengowapatali,
16Utenge chovala cha munthu amene waperekera mlendo chikole;
17Chakudya chochipeza mwachinyengo chimukomera munthu,
18Zokonzekera zimapindula utafunsira uphungu;
19Amene amanka nanena miseche amawulula zachinsinsi.
20Ngati munthu atemberera abambo ake kapena amayi ake,
21Cholowa chochipeza mofulumira poyamba,
22Usanene kuti, “Ine ndidzabwezera choyipa chimenechi!”
23Miyeso yosintha imamunyansa Yehova;
24Mayendedwe a munthu amawalamulira ndi Yehova,
25Ndi msampha kwa munthu kuyankhula mofulumira kuti “Chinthu ichi nʼchopatulika kwa Yehova,”
26Mfumu ya nzeru imapeta kwathunthu
27Mpweya wa munthu uli ngati nyale ya Yehova;
28Kukoma mtima ndi kukhulupirika ndizo zimasunga mfumu;
29Ulemerero wa achinyamata uli mu mphamvu zawo,
30Mikwingwirima yopweteka ndiyo imachotsa zoyipa,