1Ndi wabwino munthu wosauka amene amayenda mu ungwiro,
2Si bwino kuti munthu akhale wopanda nzeru;
3Uchitsiru wa munthu umamubweretsera zovuta,
4Chuma chimachulukitsa abwenzi;
5Mboni yonama sidzalephera kulangidwa;
6Anthu ambiri amafuna munthu wopatsa kuti awakomere mtima,
7Ngati munthu wosauka abale ake omwe amadana naye,
8Iye amene amapeza nzeru ndiye kuti amakonda moyo wake.
9Mboni yonama sidzalephera kulangidwa,
10Nʼkosayenera kuti chitsiru chizikhala ndi moyo wamanyado,
11Nzeru zimapangitsa munthu kukhala wosakwiya msanga;
12Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango,
13Mwana wopusa ndiye tsoka la abambo ake
14Nyumba ndi chuma ndiye cholowa chochokera kwa makolo;
15Ulesi umagonetsa tulo tofa nato
16Amene amamvera malangizo amasunga moyo wake,
17Amene amakomera mtima osauka amachita ngati wakongoletsa Yehova,
18Langa mwana wako, chiyembekezo chikanalipo;
19Munthu waukali woopsa ayenera kulandira chilango;
20Mvera uphungu ndipo landira malangizo;
21Munthu amakonzekera zambiri mu mtima mwake,
22Chimene munthu amafuna ndi chikondi chosatha;
23Kuopa Yehova kumabweretsa moyo;
24Munthu waulesi amapisa dzanja lake mʼmbale;
25Menya munthu wonyoza, ndipo anthu opanda nzeru adzachenjererapo;
26Mwana wochita ndewu ndi abambo ake ndi kuthamangitsa amayi ake,
27Mwana wanga, ukaleka kumvera malangizo,
28Mboni yopanda pake imanyoza cholungama,
29Chilango chakonzedwa kale kuti chigwere anthu oyipa,