We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 18

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 17 Miyambo Miyambo 19 →

1Munthu wokonda kukhala yekha amafunafuna zomukomera yekha;

2Chitsiru chilibe chidwi chomvetsa zinthu,

3Kuyipa mtima kukabwera, manyozonso amabwera.

4Mawu a munthu ali ngati madzi akuya,

5Si kwabwino kukondera munthu woyipa pa milandu;

6Mawu a chitsiru amautsa mkangano;

7Pakamwa pa chitsiru ndipo pamabweretsa chiwonongeko chake,

8Mawu a miseche ali ngati chakudya chokoma;

9Munthu waulesi pa ntchito yake

10Dzina la Yehova lili ngati nsanja yolimba;

11Chuma cha anthu olemera chili ngati mzinda wake wolimba;

12Chiwonongeko chisanafike, mtima wa munthu umakhala wonyada,

13Ukayankha usanamvetse bwino nkhani,

14Mtima wa munthu utha kupirira pa matenda,

15Munthu wanzeru amawonjezera nzeru zina;

16Mphatso ya munthu imamutsekulira njira

17Amene amayamba kufotokoza mlandu wake amaoneka ngati wolungama ndiye

18Kuchita maere kumathetsa mikangano;

19Mʼbale amene wamuthandiza amakhala ngati mzinda wolimba,

20Munthu amapeza bwino malingana ndi zoyankhula zake.

21Mawu ako angathe kukuphetsa kapena kukukhalitsa moyo.

22Wapeza mkazi wapeza chinthu chabwino

23Munthu wosauka amapempha

24Pali abwenzi amene chibwenzi chawo nʼchapamaso,

← Miyambo 17 Miyambo Miyambo 19 →