We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 17

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 16 Miyambo Miyambo 18 →

1Nʼkwabwino kudya mkute koma pali mtendere,

2Kapolo wanzeru adzalamulira mwana wochititsa manyazi,

3Siliva amamuyesa mʼngʼanjo ndipo golide amamuyesa mʼngʼanjo,

4Munthu woyipa amamvera malangizo oyipa;

5Iye amene amalalatira mʼmphawi amanyoza mlengi wake;

6Zidzukulu ndiye ulemu wa anthu okalamba,

7Kuyankhula bwino sikuyenerana ndi chitsiru,

8Chiphuphu chili ngati mankhwala amwayi kwa wochiperekayo;

9Iye amene amakhululukira zolakwa za wina, amafunitsitsa chikondi;

10Munthu wanzeru amamva kamodzi kokha,

11Munthu woyipa maganizo ake ali pa kuwukira basi;

12Nʼkwabwino kukumana ndi chimbalangondo cholandidwa ana ake

13Ngati munthu abwezera choyipa kusinthana ndi zabwino,

14Chiyambi cha mikangano chili ngati kukhamulira madzi,

15Kumasula munthu wolakwa kapena kumanga munthu wosalakwa,

16Ndalama zogulira nzeru zili ndi phindu lanji mʼmanja mwa chitsiru

17Bwenzi lako limakukonda nthawi zonse,

18Munthu wopanda nzeru amavomereza zopereka chikole

19Wokonda zolakwa amakonda mkangano,

20Munthu wamtima woyipa zinthu sizimuyendera bwino;

21Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake,

22Mtima wosangalala uli ngati mankhwala abwino,

23Munthu woyipa amalandira chiphuphu chamseri

24Munthu wozindikira zinthu, maso ake amakhala pa nzeru,

25Mwana wopusa amamvetsa chisoni abambo ake

26Sibwino kulipitsa munthu wosalakwa,

27Munthu wosunga pakamwa ndiye wodziwa zinthu,

28Ngakhale chitsiru chimakhala ngati chanzeru chikakhala chete;

← Miyambo 16 Miyambo Miyambo 18 →