We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 15

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 14 Miyambo Miyambo 16 →

1Kuyankha kofatsa kumathetsa mkwiyo,

2Munthu wanzeru amayankhula zinthu za nzeru,

3Maso a Yehova ali ponseponse,

4Kuyankhula kodekha kuli ngati mtengo wopatsa moyo,

5Chitsiru chimanyoza mwambo wa abambo ake,

6Munthu wolungama amakhala ndi chuma chambiri,

7Pakamwa pa anthu anzeru pamafalitsa nzeru;

8Nsembe za anthu oyipa zimamunyansa Yehova,

9Ntchito za anthu oyipa zimamunyansa Yehova

10Amene amasiya njira yabwino adzalangidwa koopsa.

11Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova,

12Wonyoza sakonda kudzudzulidwa;

13Mtima wokondwa umachititsa nkhope kukhala yachimwemwe,

14Mtima wa munthu wozindikira zinthu umafunafuna nzeru,

15Munthu woponderezedwa masiku ake onse amakhala oyipa,

16Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono nʼkumaopa Yehova,

17Kuli bwino kudyera ndiwo zamasamba pamene pali chikondi,

18Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano,

19Njira ya munthu waulesi ndi yowirira ndi mtengo waminga,

20Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake,

21Uchitsiru umakondweretsa munthu wopanda nzeru,

22Popanda uphungu zolinga zako munthu zimalephereka,

23Munthu amakondwera ndi kuyankha koyenera,

24Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo

25Yehova amapasula nyumba ya munthu wonyada

26Maganizo a anthu oyipa amamunyansa Yehova,

27Munthu wofuna phindu mwachinyengo amavutitsa banja lake,

28Munthu wolungama amaganizira za mmene ayankhire,

29Yehova amakhala kutali ndi anthu oyipa,

30Kuwala kwa maso kumasangalatsa mtima

31Womvera mawu a chidzudzulo amene apatsa moyo

32Amene amanyoza mwambo amadzinyoza yekha,

33Kuopa Yehova kumaphunzitsa munthu nzeru,

← Miyambo 14 Miyambo Miyambo 16 →