We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Miyambo 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Miyambo 13 Miyambo Miyambo 15 →

1Mkazi wanzeru amamanga banja lake,

2Amene amayenda molungama amaopa Yehova,

3Kuyankhula kwa chitsiru kumamuyitanira ndodo pa msana,

4Pakasowa ngʼombe zolima gome limakhala lopanda chakudya,

5Mboni yokhulupirika sinama,

6Wonyoza anzake amafunafuna nzeru koma osayipeza,

7Khala kutali ndi munthu wopusa

8Nzeru za munthu wochenjera zagona pakuzindikira njira zake.

9Zitsiru zimanyoza za kulapa machimo, awo,

10Mtima uliwonse umadziwa wokha zowawa zake,

11Nyumba ya munthu woyipa idzapasuka,

12Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu,

13Ngakhale poseka mtima utha kumva kuwawa,

14Munthu wosakhulupirika adzalandira zogwirizana ndi ntchito yake,

15Munthu wopusa amakhulupirira chilichonse,

16Munthu wanzeru amaopa Mulungu ndipo amapewa zoyipa,

17Munthu wopsa mtima msanga amachita zinthu za uchitsiru,

18Anthu opusa amalandira uchitsiru,

19Anthu oyipa adzagwada pamaso pa anthu abwino,

20Munthu wosauka ngakhale anansi ake omwe amamuda,

21Wonyoza mnansi wake ndi wochimwa

22Kodi amene amakonzekera zoyipa sasochera?

23Ntchito iliyonse imakhala ndi phindu,

24Chipewa chaulemu cha anthu a nzeru ndi chuma chawo chomwe,

25Mboni yokhulupirika imapulumutsa miyoyo,

26Amene amaopa Yehova ali ndi chitetezo chokwanira

27Kuopa Yehova ndiye kasupe wamoyo,

28Gulu lalikulu la anthu ndiye ulemerero wa mfumu,

29Munthu wosapsa mtima msanga amamvetsa zinthu kwambiri,

30Mtima wodekha umapatsa thupi moyo,

31Amene amapondereza mʼmphawi amanyoza mlengi wake,

32Anthu oyipa adzakanthidwa chifukwa cha ntchito zawo zomwe,

33Nzeru zimakhala mu mtima mwa anthu omvetsa zinthu,

34Chilungamo chimakweza mtundu wa anthu,

35Mfumu imasangalatsidwa ndi wantchito wanzeru,

← Miyambo 13 Miyambo Miyambo 15 →