1Iwe Israeli, usakondwere;
2Malo opunthira tirigu ndi malo opsinyira mphesa sadzadyetsa anthu;
3Sadzakhalanso mʼdziko la Yehova.
4Iwo sadzaperekanso chopereka cha chakumwa kwa Yehova,
5Kodi mudzachita chiyani pa tsiku la maphwando anu oyikika;
6Ngakhale iwo atathawa chiwonongeko,
7Masiku achilango akubwera,
8Mneneri pamodzi ndi Mulungu wanga
9Iwo azama mu zachinyengo
10“Pamene ndinamupeza Israeli
11Ulemerero wa Efereimu udzawuluka ngati mbalame.
12Ngakhale atalera ana
13Ndaona Efereimu ngati Turo,
14Inu Yehova, muwapatse.
15“Chifukwa cha zoyipa zawo zonse ku Giligala,
16Efereimu wathedwa,
17Mulungu wanga adzawakana