1Israeli anali mpesa wotambalala;
2Mtima wawo ndi wonyenga
3Pamenepo anthuwo adzanena kuti, “Ife tilibe mfumu
4Mafumu amalonjeza zambiri,
5Anthu amene amakhala mu Samariya akuchita mantha
6Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya
7Samariya ndi mfumu yake adzatengedwa kupita kutali
8Malo opembedzerako mafano a ku Aveni adzawonongedwa.
9“Iwe Israeli, wachimwa kuyambira mʼmasiku a Gibeya,
10Pamene ndifunire, ndidzalanga anthuwo;
11Efereimu ndi mwana wangʼombe wamkazi wophunzitsidwa
12Mufese nokha chilungamo
13Koma inu munadzala zolakwa,
14phokoso lankhondo lidzamveka pakati pa anthu anga
15Momwemonso zidzakuchitikira, iwe Beteli