1“Israeli ali mwana, ndinamukonda,
2Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana
3Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda,
4Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu
5“Sadzabwerera ku Igupto,
6Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo,
7Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine.
8“Kodi ndingakusiye bwanji iwe Efereimu?
9Sindidzalola kuti ndikulange ndi mkwiyo wanga woopsa,
10Iwo adzatsatira Yehova;
11Adzabwera akunjenjemera
12Efereimu wandizungulira ndi mabodza,