1Efereimu amadya mpweya;
2Yehova akuyimba mlandu Yuda;
3Akali mʼmimba mwa amayi ake, Yakobo anagwira chidendene cha mʼbale wake;
4Yakobo analimbana ndi mngelo ndipo anapambana;
5Yehova Mulungu Wamphamvuzonse,
6Koma inu muyenera kubwerera kwa Mulungu wanu;
7Munthu wamalonda amagwiritsa ntchito masikelo achinyengo;
8Efereimu amadzitama ponena kuti,
9“Ine ndine Yehova Mulungu wako
10Ndinayankhula ndi aneneri,
11Kodi Giliyadi ndi woyipa?
12Yakobo anathawira ku dziko la Aramu,
13Yehova anagwiritsa ntchito mneneri kuti atulutse Israeli mu Igupto;
14Koma Efereimu wamukwiyitsa kwambiri.