We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Hoseya 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Hoseya 12 Hoseya Hoseya 14 →

1Kale Efereimu ankati akayankhula, anthu ankanjenjemera;

2Tsopano akunka nachimwirachimwirabe;

3Choncho adzakhala ngati nkhungu yammawa,

4Koma Ine ndine Yehova Mulungu wanu,

5Ndinakusamalira mʼchipululu,

6Pamene ndinawadyetsa, iwo anakhuta;

7Motero ndidzawalumphira ngati mkango,

8Ngati chimbalangondo cholandidwa ana ake,

9“Iwe Israeli, wawonongedwa,

10Kodi mfumu yako ili kuti, kuti ikupulumutse?

11Choncho Ine ndinakupatsani mfumu mwachipseramtima,

12Kulakwa kwa Efereimu kwasungidwa,

13Zowawa zonga za mayi pa nthawi yobala mwana zamugwera,

14“Ndidzawapulumutsa ku mphamvu ya manda;

15ngakhale Efereimu akondwe pakati pa abale ake,

16Anthu a ku Samariya adzalangidwa chifukwa cha zolakwa zawo,

← Hoseya 12 Hoseya Hoseya 14 →