1Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako.
2Bweretsani zopempha zanu
3Asiriya sangatipulumutse;
4Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo
5Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli
6mphukira zake zidzakula.
7Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake.
8Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano?
9Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi.