1“Ika lipenga pakamwa pako.
2Israeli akulirira kwa Ine kuti,
3Koma Israeli wakana zabwino;
4Amalonga mafumu mosatsata kufuna kwanga.
5Iwe Samariya, taya fano lako la mwana wangʼombe!
6Mafanowa ndi ochokera ku Israeli!
7“Aisraeli amadzala mphepo
8Israeli wamezedwa,
9Pakuti iwo anapita ku Asiriya
10Ngakhale wadzigulitsa pakati pa mitundu ya anthu,
11“Ngakhale Efereimu anamanga maguwa ambiri a nsembe zoperekedwa chifukwa cha tchimo,
12Ndinawalembera zinthu zambiri za malamulo anga,
13Amapereka nsembe za nyama kwa Ine
14Israeli wayiwala Mlengi wake