1Pamene ndichiritsa Israeli,
2Koma sazindikira kuti Ine
3“Anthuwa amasangalatsa mfumu ndi zoyipa zawozo,
4Onsewa ndi anthu azigololo,
5Pa tsiku la chikondwerero cha mfumu yathu
6Mitima yawo ili ngati uvuni;
7Onsewa ndi otentha ngati uvuni,
8“Efereimu wasakanikirana ndi mitundu ya anthu ena;
9Alendo atha mphamvu zake,
10Kunyada kwake Israeli kukumutsutsa,
11“Efereimu ali ngati nkhunda
12Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga;
13Tsoka kwa iwo,
14Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima,
15Ine ndinawaphunzitsa ndikuwalimbitsa,
16Iwo satembenukira kwa Wammwambamwamba;