We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Hoseya 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Hoseya 6 Hoseya Hoseya 8 →

1Pamene ndichiritsa Israeli,

2Koma sazindikira kuti Ine

3“Anthuwa amasangalatsa mfumu ndi zoyipa zawozo,

4Onsewa ndi anthu azigololo,

5Pa tsiku la chikondwerero cha mfumu yathu

6Mitima yawo ili ngati uvuni;

7Onsewa ndi otentha ngati uvuni,

8“Efereimu wasakanikirana ndi mitundu ya anthu ena;

9Alendo atha mphamvu zake,

10Kunyada kwake Israeli kukumutsutsa,

11“Efereimu ali ngati nkhunda

12Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga;

13Tsoka kwa iwo,

14Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima,

15Ine ndinawaphunzitsa ndikuwalimbitsa,

16Iwo satembenukira kwa Wammwambamwamba;

← Hoseya 6 Hoseya Hoseya 8 →