1Wodzathira nkhondo akubwera
2Yehova adzabwezeretsa ulemerero wa Yakobo
3Zishango za ankhondo ake ndi zofiira;
4Magaleta akuthamanga mʼmisewu
5Iye akuyitanitsa asilikali ake wolemekezeka,
6Atsekula zipata zotchinga madzi a mu mtsinje
7Zatsimikizika kuti mzinda
8Ninive ali ngati dziwe,
9Funkhani siliva!
10Iye wawonongedwa, wafunkhidwa ndipo wavulidwa!
11Kodi tsopano dzenje la mikango lili kuti,
12Mkango waumuna unkapha nyama yokwanira ana ake
13Yehova Wamphamvuzonse akuti,