1Uthenga wonena za Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi.
2Yehova ndi Mulungu wansanje
3Yehova sakwiya msanga koma ndi wa mphamvu yayikulu;
4Amalamulira nyanja ndipo imawuma;
5Mapiri amagwedera pamaso pake
6Ndani angathe kuyima pamaso pake Iye akalusa?
7Yehova ndi wabwino,
8koma ndi madzi achigumula choopsa
9Chiwembu chilichonse chimene akukonzekera kumuchitira Yehova
10Iwo adzakodwa mu ziyangoyango za minga
11Kwa iwe, Ninive, kunachokera munthu wa cholinga choyipa,
12Yehova akuti,
13Tsopano ndidzathyola goli lake pa khosi lako
14Yehova walamulira za iwe, Ninive kuti,
15Taonani, pa phiripo,