We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Nahumu 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Nahumu Nahumu 2 →

1Uthenga wonena za Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi.

2Yehova ndi Mulungu wansanje

3Yehova sakwiya msanga koma ndi wa mphamvu yayikulu;

4Amalamulira nyanja ndipo imawuma;

5Mapiri amagwedera pamaso pake

6Ndani angathe kuyima pamaso pake Iye akalusa?

7Yehova ndi wabwino,

8koma ndi madzi achigumula choopsa

9Chiwembu chilichonse chimene akukonzekera kumuchitira Yehova

10Iwo adzakodwa mu ziyangoyango za minga

11Kwa iwe, Ninive, kunachokera munthu wa cholinga choyipa,

12Yehova akuti,

13Tsopano ndidzathyola goli lake pa khosi lako

14Yehova walamulira za iwe, Ninive kuti,

15Taonani, pa phiripo,

Nahumu Nahumu 2 →