1Tsoka kwa mzinda wopha anthu,
2Kulira kwa zikwapu,
3Kuthamanga kwa anthu okwera pa akavalo,
4Zonsezi ndi chifukwa cha zilakolako za mkazi wachiwerewere,
5Yehova Wamphamvuzonse akuti,
6Ndidzakuthira zonyansa,
7Onse amene adzakuona adzakuthawa ndipo adzati,
8Kodi ndiwe wopambana Tebesi,
9Mphamvu zake zinali Kusi ndi Igupto,
10Komabe anthu a ku Tebesi anagwidwa
11Iwenso Ninive udzaledzera;
12Malo ako onse otetezedwa ali ngati mitengo ya mkuyu
13Tayangʼana ankhondo ako,
14Tungani madzi woti mudzamwe nthawi ya kuzunguliridwa kwanu,
15Kumeneko moto udzakupserezani;
16Mwachulukitsa chiwerengero cha anthu a malonda anu
17Akalonga ako ali ngati dzombe,
18Iwe mfumu ya ku Asiriya,
19Palibe chimene chingachize bala lako;