We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mika 6

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Mika 5 Mika Mika 7 →

1Tamverani zimene Yehova akunena:

2Imvani mlandu wa Yehova, inu mapiri;

3“Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani?

4Ine ndinakutulutsani ku dziko la Igupto

5Anthu anga, kumbukirani

6Kodi ndidzatenga chiyani kupita nacho pamaso pa Yehova

7Kodi Yehova adzakondwera ndi nkhosa zazimuna 1,000,

8Munthu iwe, Yehova wakuonetsa kale chimene chili chabwino.

9Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzinda

10Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwala

11Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo,

12Anthu ake olemera amachita zachiwawa;

13Choncho, ndayamba kukuwonongani,

14Mudzadya, koma simudzakhuta;

15Mudzadzala, koma simudzakolola.

16Inu mwatsatira malangizo a Omuri

← Mika 5 Mika Mika 7 →