1Tamverani zimene Yehova akunena:
2Imvani mlandu wa Yehova, inu mapiri;
3“Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani?
4Ine ndinakutulutsani ku dziko la Igupto
5Anthu anga, kumbukirani
6Kodi ndidzatenga chiyani kupita nacho pamaso pa Yehova
7Kodi Yehova adzakondwera ndi nkhosa zazimuna 1,000,
8Munthu iwe, Yehova wakuonetsa kale chimene chili chabwino.
9Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzinda
10Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwala
11Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo,
12Anthu ake olemera amachita zachiwawa;
13Choncho, ndayamba kukuwonongani,
14Mudzadya, koma simudzakhuta;
15Mudzadzala, koma simudzakolola.
16Inu mwatsatira malangizo a Omuri