We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mika 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Mika 6 Mika

1Tsoka ine!

2Anthu opembedza atha mʼdziko;

3Manja awo onse ndi aluso pochita zoyipa;

4Munthu wabwino kwambiri pakati pawo ali ngati mtengo waminga,

5Usadalire mnansi;

6Pakuti mwana wamwamuna akunyoza abambo ake,

7Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo,

8Iwe mdani wanga, usandiseke!

9Ndidzapirira mkwiyo wa Yehova,

10Ndipo mdani wanga adzaona zimenezi

11Idzafika nthawi yomanganso makoma anu,

12Nthawi imeneyo anthu adzabwera kwa inu

13Dziko lapansi lidzasanduka chipululu

14Wetani anthu anu ndi ndodo yanu yowateteza,

15“Ndidzawaonetsa zodabwitsa zanga,

16Mitundu ya anthu idzaona zimenezi ndipo idzachita manyazi,

17Adzabwira fumbi ngati njoka,

18Kodi alipo Mulungu wofanana nanu,

19Inu mudzatichitiranso chifundo;

20Mudzakhala wokhulupirika kwa Yakobo,

← Mika 6 Mika