We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mika 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Mika 4 Mika Mika 6 →

1Iwe mzinda wa anthu ankhondo, sonkhanitsa anthu ako ankhondo,

2“Koma iwe Betelehemu Efurata,

3Nʼchifukwa chake Israeli adzasiyidwa

4Iye adzalimbika, ndipo adzaweta nkhosa zake

5Ndipo Iye adzakhala mtendere wawo.

6Iwo adzagonjetsa dziko la Asiriya ndi lupanga,

7Otsalira a Yakobo adzakhala

8Otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu ya anthu,

9Mudzagonjetsa adani anu,

10Yehova akuti,

11Ndidzawononga mizinda ya mʼdziko mwanu

12Ndidzawononga ufiti wanu

13Ndidzawononga mafano anu osema

14Ndidzazula mitengo ya mafano a Asera imene ili pakati panu,

15Ndidzayilanga mwaukali ndi mokwiya

← Mika 4 Mika Mika 6 →