1Iwe mzinda wa anthu ankhondo, sonkhanitsa anthu ako ankhondo,
2“Koma iwe Betelehemu Efurata,
3Nʼchifukwa chake Israeli adzasiyidwa
4Iye adzalimbika, ndipo adzaweta nkhosa zake
5Ndipo Iye adzakhala mtendere wawo.
6Iwo adzagonjetsa dziko la Asiriya ndi lupanga,
7Otsalira a Yakobo adzakhala
8Otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu ya anthu,
9Mudzagonjetsa adani anu,
10Yehova akuti,
11Ndidzawononga mizinda ya mʼdziko mwanu
12Ndidzawononga ufiti wanu
13Ndidzawononga mafano anu osema
14Ndidzazula mitengo ya mafano a Asera imene ili pakati panu,
15Ndidzayilanga mwaukali ndi mokwiya