1Tsoka kwa amene amakonzekera chiwembu,
2Amasirira minda ndi kuyilanda,
3Nʼchifukwa chake Yehova akuti,
4Tsiku limenelo anthu adzakuchitani chipongwe;
5Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova
6Aneneri awo amanena kuti, “Usanenere!
7Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena:
8Posachedwapa anthu anga andiwukira
9Mumatulutsa akazi a anthu anga
10Nyamukani, chokani!
11Ngati munthu wabodza ndi wachinyengo abwera nʼkunena kuti,
12“Inu banja la Yakobo, ndidzakusonkhanitsani nonse;
13Amene adzawapulumutse adzayenda patsogolo pawo;